Eksodo 6:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nawalangiza za ana a Israele, ndi za Farao mfumu ya Aejipito, kuti atulutse ana a Israele m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nawalangiza za ana a Israele, ndi za Farao mfumu ya Aejipito, kuti atulutse ana a Israele m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma Chauta adalamula Mose ndi Aroni kuti akauze Aisraele ndi Farao mfumu ya ku Ejipito, kuti Aisraelewo ayenera kutuluka m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndipo Yehova analamula Mose ndi Aaroni kuti awuze Aisraeli ndi Farao mfumu ya Igupto kuti Aisraeli ayenera kutuluka mʼdziko la Igupto. Onani mutuwo |