Eksodo 6:11 - Buku Lopatulika11 Lowa, lankhula ndi Farao mfumu ya Aejipito, kuti alole ana a Israele atuluke m'dziko lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Lowa, lankhula ndi Farao mfumu ya Aejipito, kuti alole ana a Israele atuluke m'dziko lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Pita kamuuze Farao, mfumu ya ku Ejipito, kuti aŵalole Aisraele kutuluka m'dziko mwake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Pita ukawuze Farao mfumu ya Igupto kuti awalole Aisraeli atuluke mʼdziko lake.” Onani mutuwo |