Eksodo 5:12 - Buku Lopatulika12 Pamenepo anthuwo anabalalika m'dziko lonse la Ejipito kufuna chiputu ngati udzu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pamenepo anthuwo anabalalika m'dziko lonse la Ejipito kufuna chiputu ngati udzu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Motero anthu aja adamwazikira m'dziko lonse la Ejipito kukafunafuna udzuwo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Kotero anthuwo anamwazikana mʼdziko lonse la Igupto kukamweta udzu. Onani mutuwo |