Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 5:11 - Buku Lopatulika

11 Mukani inu nokha, dzifunireni udzu komwe muupeza; pakuti palibe kanthu kadzachepa pa ntchito yanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Mukani inu nokha, dzifunireni udzu komwe muupeza; pakuti palibe kanthu kadzachepa pa ntchito yanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Muzidzimwetera nokha kulikonse komwe mungaupeze. Koma chiŵerengero cha njerwa ndi chonchija.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Mʼmalo mwake mupite mukadzimwetere udzu kulikonse kumene mungawupeze. Komabe ntchito yanu sichepetsedwa.’ ”

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 5:11
3 Mawu Ofanana  

Ndipo akufulumiza anthu ndi akapitao ao anatuluka, nanena ndi anthu ndi kuti, Atero Farao, Kulibe kukupatsani udzu.


Pamenepo anthuwo anabalalika m'dziko lonse la Ejipito kufuna chiputu ngati udzu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa