Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 40:38 - Buku Lopatulika

38 Pakuti mtambo wa Yehova unakhala pa chihema msana, ndi usiku munali moto m'menemo, pamaso pa mbumba yonse ya Israele, m'maulendo ao onse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Pakuti mtambo wa Yehova unakhala pa Kachisi msana, ndi usiku munali moto m'menemo, pamaso pa mbumba yonse ya Israele, m'maulendo ao onse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Unkakhala pachihemapo masana, usiku mumtambomo munkayaka moto, ndipo Aisraele onse ankatha kuupenya. Zinkatero pa ulendo wao wonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Kotero mtambo wa Yehova unkakhala pamwamba pa chihema usana, ndi mtambo wamoto umakhala usiku, pamaso pa nyumba yonse ya Israeli pa masiku onse aulendo wawo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 40:38
10 Mawu Ofanana  

Pakuti sindinakhale m'nyumba kuyambira tsiku lija ndinatulutsa ana a Israele ku Ejipito kufikira lero lomwe, koma ndinayenda m'chihema ndi m'nyumba wamba.


Anayala mtambo uwaphimbe; ndi moto uunikire usiku.


Ndipo msana anawatsogolera ndi mtambo ndi usiku wonse ndi kuunika kwa moto.


Ndipo Yehova anawatsogolera usana ndi mtambo njo kuwatsogolera m'njira; ndi usiku ndi moto njo, wakuwawalitsira; kuti ayende usana ndi usiku;


sanachotse mtambo usana, kapena mtambo wamoto usiku, pamaso pa anthu.


Ndipo mtambo wa Yehova unali pamwamba pao msana, pakuyenda iwo kuchokera kuchigono.


Asasiyeko kufikira m'mawa, kapena kuthyolapo fupa; auchite monga mwa lemba lonse la Paska.


Ndipo tsiku loutsa Kachisi mtambo unaphimba Kachisi, ndiwo chihema chokomanako; ndicho chihema chaumboni, ndipo madzulo padaoneka pa Kachisi ngati moto, kufikira m'mawa.


Kudatero kosalekeza; mtambo umachiphimba, ndi moto umaoneka usiku.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa