Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 40:37 - Buku Lopatulika

37 koma ukapanda kukwera mtambo, samayenda ulendo wao kufikira tsiku loti wakwera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 koma ukapanda kukwera mtambo, samayenda ulendo wao kufikira tsiku loti wakwera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Koma mtambowo ukapanda kuchoka, Aisraele sankachokanso pachigonopo. Ankadikira tsiku lakuti mtambo wachokapo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Koma ngati mtambo sunachoke, iwo sankasamukanso mpaka tsiku limene udzachoke.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 40:37
2 Mawu Ofanana  

Nyengo zanga zili m'manja mwanu, mundilanditse m'manja a adani anga, ndi kwa iwo akundilondola ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa