Eksodo 40:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo anaika guwa la nsembe lagolide m'chihema chokomanako chakuno cha nsalu yotchinga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo anaika guwa la nsembe lagolide m'chihema chokomanako chakuno cha nsalu yotchinga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 M'chihema chamsonkhanomo adaikamo guwa lagolide patsogolo pa nsalu yochinga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Mose anayika guwa la golide mu tenti ya msonkhano patsogolo pa katani Onani mutuwo |