Eksodo 40:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo kunali, mwezi woyamba wa chaka chachiwiri, tsiku loyamba la mwezi, anautsa chihema, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo kunali, mwezi woyamba wa chaka chachiwiri, tsiku loyamba la mwezi, anautsa Kachisi, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Motero pa tsiku loyamba la mwezi woyamba chaka chachiŵiri, malo opatulika adautsidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Kotero anayimika chihema tsiku loyamba la mwezi woyamba mʼchaka chachiwiri. Onani mutuwo |