Eksodo 40:13 - Buku Lopatulika13 Nuveke Aroni chovala zopatulikazo; ndi kumdzoza, ndi kumpatula andichitire Ine ntchito ya nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Nuveke Aroni chovala zopatulikazo; ndi kumdzoza, ndi kumpatula andichitire Ine ntchito ya nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Aroniyo umuveke zovala zopatulika. Umdzoze, ndipo umpatule kuti akhale wansembe wonditumikira Ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kenaka umuveke Aaroni zovala zopatulika, umudzoze ndi kumupatula kotero kuti athe kunditumikira monga wansembe. Onani mutuwo |