Eksodo 4:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo ukalankhule naye, ndi kumpangira mau; ndipo Ine ndidzakhala m'kamwa mwako, ndi m'kamwa mwake, ndipo ndidzakuphunzitsani inu chimene mukachite. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo ukalankhule naye, ndi kumpangira mau; ndipo Ine ndidzakhala m'kamwa mwako, ndi m'kamwa mwake, ndipo ndidzakuphunzitsani inu chimene mukachite. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Udzalankhula naye iyeyo ndi kumuuza zoti akanene. Ndidzakuthandizani kulankhula nonse aŵirinu, ndipo ndidzakuuzaninso zoti mukachite. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Iwe udzayankhula naye ndi kumuwuza mawu oti akanene. Ine ndidzakuthandizani kuyankhula nonse awirinu ndi kukulangizani zoti mukachite. Onani mutuwo |