Eksodo 4:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Mose anati kwa Yehova, Mverani, Ambuye, ine ndine munthu wosowa ponena, kapena dzulo, kapena kale, kapena chilankhulire Inu ndi kapolo wanu, pakuti ndine wa m'kamwa molemera, ndi wa lilime lolemera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Mose anati kwa Yehova, Mverani, Ambuye, ine ndine munthu wosowa ponena, kapena dzulo, kapena kale, kapena chilankhulire Inu ndi kapolo wanu, pakuti ndine wa m'kamwa molemera, ndi wa lilime lolemera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Mose adati, “Pepani Chauta, ndapota nanu, ine sindidziŵa kulankhula bwino chiyambire kale, kapena kuyambira paja mwayamba kulankhula nane mtumiki wanune. Lilime langa ndi lolemera, ndine wachibwibwi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mose anati kwa Yehova, “Chonde Ambuye, chikhalire ine ndakhala munthu wosatha kuyankhula bwino. Ngakhale tsopano pamene mukundiyankhula, lilime langa ndi lolemera. Ndine wachibwibwi.” Onani mutuwo |