Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 39:23 - Buku Lopatulika

23 ndi pakati pake polowa mutu, ngati polowa pa malaya ochingirizira, ndipo anabinyira pozungulira polowa pake, pangang'ambike.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 ndi pakati pake polowa mutu, ngati polowa pa malaya ochingirizira, ndipo anabinyira pozungulira polowa pake, pangang'ambike.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Mkanjowo unali ndi popisa mutu, ndipo maonekedwe ake anali ngati popisa mutu pa malaya. M'mbali mwake kuzungulira, munali mosokerera bwino, kuti ungang'ambike.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Mkanjowo unali ndi malo opisapo mutu pakati pakepo. Pa chibowopo panali chibandi chosokedwa mochita ngati kuluka monga muja akhalira malaya kuti chibowocho chilimbe, chisangʼambike.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 39:23
2 Mawu Ofanana  

Ndipo polowa mutu pakhale pakati pake; pakhale mkawo pozungulira polowa pake, wa ntchito yoomba, ngati polowa pa malaya otchinjiriza, pangang'ambike.


Napangira pa mkawo wa mwinjiro makangaza a lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa