Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 39:22 - Buku Lopatulika

22 Ndipo anaomba mwinjiro wa efodi, ntchito yoomba ya lamadzi lokha;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ndipo anaomba mwinjiro wa efodi, ntchito yoomba ya lamadzi lokha;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Adapanga mkanjo wake wa efodi, woombedwa ndi nsalu yobiriŵira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Anayipangira efodiyo mkanjo wamtundu wa mtambo, wolukidwa ndi mmisiri waluso.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 39:22
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anamanga chapachifuwa pa mphete zake ndi mphete za efodi ndi mkuzi wamadzi, kuti chikhale pa mpango wa efodi, ndi kuti chapachifuwa chisamasuke paefodi; monga Yehova anamuuza Mose.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa