Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 38:15 - Buku Lopatulika

15 momwemonso pa mbali ina: pa mbali ino ndi pa mbali ina ya chipata cha pabwalo panali nsalu zotchingira za mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zitatu, ndi makamwa ake atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 momwemonso pa mbali ina: pa mbali yino ndi pa mbali ina ya chipata cha pabwalo panali nsalu zochingira za mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zitatu, ndi makamwa ake atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Pa mbali inayo panali chimodzimodzi. Choncho pa mbali zonse ziŵirizo za chipata choloŵera ku bwalo chija, panali nsalu zochinga, zotalika mamita asanu ndi aŵiri, zokhala ndi nsanamira zitatu ndi masinde atatu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 polowera mʼbwalo panali nsalu yotchinga ya mamita asanu ndi awiri pamodzi ndi mizati itatu ndi matsinde atatu.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 38:15
2 Mawu Ofanana  

Nsalu zotchingira za pa mbali imodzi ya chipata nza mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zitatu, ndi makamwa ake atatu;


Nsalu zotchingira zonse za pabwalo pozungulira zinali za bafuta wa thonje losansitsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa