Eksodo 38:16 - Buku Lopatulika16 Nsalu zotchingira zonse za pabwalo pozungulira zinali za bafuta wa thonje losansitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Nsalu zochingira zonse za pabwalo pozungulira zinali za bafuta wa thonje losansitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Nsalu zonse zochinga kuzungulira bwalolo zinali za bafuta wosalala ndi wopikidwa bwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Katani yonse yotchinga kuzungulira chihema inali yofewa, yosalala ndi yolukidwa bwino. Onani mutuwo |