Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 38:14 - Buku Lopatulika

14 Nsalu zotchingira za pa mbali imodzi ya chipata nza mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zitatu, ndi makamwa ake atatu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Nsalu zochingira za pa mbali imodzi ya chipata nza mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zitatu, ndi makamwa ake atatu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Panali nsalu zochinga pa mbali imodzi ya chipata, zotalika mamita asanu ndi aŵiri, zokhala ndi nsanamira zake zitatu ndi masinde atatu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Mbali imodzi yachipata kunali nsalu yotchinga yotalika mamita asanu ndi awiri, mizati itatu ndi matsinde atatu,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 38:14
3 Mawu Ofanana  

Ndi nsalu zotchingira za pa mbali imodzi ya kuchipata zikhale za mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zikhale zitatu, ndi makamwa ao atatu.


Ndi pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mikono makumi asanu.


momwemonso pa mbali ina: pa mbali ino ndi pa mbali ina ya chipata cha pabwalo panali nsalu zotchingira za mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zitatu, ndi makamwa ake atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa