Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 38:13 - Buku Lopatulika

13 Ndi pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mikono makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndi pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mikono makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Pa mbali inayo yakuvuma panalinso mamita 23.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Mbali yakummawa, kotulukira dzuwa, inalinso yotalika mamita 23.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 38:13
2 Mawu Ofanana  

Ndi pa mbali ya kumadzulo panali nsalu zotchingira za mikono makumi asanu, nsichi zake khumi, ndi makamwa ake khumi; zokowera za nsichi ndi mitanda yake yasiliva.


Nsalu zotchingira za pa mbali imodzi ya chipata nza mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zitatu, ndi makamwa ake atatu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa