Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 37:28 - Buku Lopatulika

28 Ndipo anazipanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi golide.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ndipo anazipanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi golide.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Mphikozo adazipanga ndi matabwa a mtengo wa kasiya, naikuta ndi golide.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Anapanga mizati yamtengo wa mkesha ndipo anayikuta ndi golide.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 37:28
3 Mawu Ofanana  

ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Ndipo analipangira mphete ziwiri zagolide pansi pa mkombero wake, pangodya zake ziwiri, pa mbali zake ziwiri, zikhale zopisamo mphiko kulinyamulira nazo.


Anapanganso mafuta opatulika akudzoza nao, ndi chofukiza choona cha fungo lokoma, mwa machitidwe a wosakaniza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa