Eksodo 37:29 - Buku Lopatulika29 Anapanganso mafuta opatulika akudzoza nao, ndi chofukiza choona cha fungo lokoma, mwa machitidwe a wosakaniza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Anapanganso mafuta opatulika akudzoza nao, ndi chofukiza choona cha fungo lokoma, mwa machitidwe a wosanganiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Adapanganso mafuta oyera odzozera, ndiponso zofukizira za fungo lokoma. Mapangidwe ake adachita monga momwe ankachitira mmisiri wopanga zonunkhira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Iwo anapanganso mafuta opatulika odzozera ndi zofukiza za fungo lokoma kwambiri. Iyi inali ntchito ya mʼmisiri waluso lopanga zonunkhiritsa. Onani mutuwo |