Eksodo 37:24 - Buku Lopatulika24 Anachipanga ichi ndi zipangizo zake zonse za talente wa golide woona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Anachipanga ichi ndi zipangizo zake zonse za talente wa golide woona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Popanga choikaponyalecho, pamodzi ndi zipangizo zake zonsezo, adagwiritsa ntchito makilogaramu 34 a golide wabwino kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Iwo anapanga choyikapo nyale ndi zipangizo zake zonse zagolide wabwino kwambiri wolemera makilogalamu 34. Onani mutuwo |