Eksodo 37:19 - Buku Lopatulika19 pa mphanda imodzi panali zikho zitatu zopangika ngati katungurume, mutu ndi duwa; ndi pa mphanda ina zikho zitatu zopangika ngati katungurume, mutu ndi duwa zinatero mphanda zisanu ndi imodzi zotuluka m'choikaponyali. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 pa mphanda imodzi panali zikho zitatu zopangika ngati katungurume, mutu ndi luwa; ndi pa mphanda ina zikho zitatu zopangika ngati katungurume, mutu ndi luwa zinatero mphanda zisanu ndi imodzi zotuluka m'choikapo nyali. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Iliyonse mwa nthambizo inali ndi maluŵa atatu, opangidwa ngati maluŵa amtowo, okhala ndi nkhunje ndi maluŵa ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Zikho zitatu zokhala ngati za maluwa amtowo, mphukira ndi duwa zinali pa mphanda yoyamba. Pa mphanda yachiwiri panalinso zikho zitatu zokhala ngati za maluwa amtowo, mphukira ndi duwa. Ndipo mphanda zonse zisanu ndi imodzi zinali chimodzimodzi ndipo zinatuluka mʼchoyikapo nyalecho. Onani mutuwo |