Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:9 - Buku Lopatulika

9 Utali wake wa nsalu yophimba imodzi ndiwo mikono makumi awiri kudza isanu ndi itatu, ndi kupingasa kwake kwa nsalu imodzi mikono inai; nsalu zonse zinafanana muyeso wao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Utali wake wa nsalu yophimba imodzi ndiwo mikono makumi awiri kudza isanu ndi itatu, ndi kupingasa kwake kwa nsalu imodzi mikono inai; nsalu zonse zinafanana muyeso wao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 M'litali mwa nsalu iliyonse munali mamita 13, ndipo muufupi mwake munali masentimita 183. Zonsezo zinali zofanana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Nsalu zonse zinali zofanana. Mulitali mwake zinali mamita khumi ndi atatu, mulifupi mamita awiri.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:9
2 Mawu Ofanana  

Ndipo analumikiza nsalu zisanu ina ndi inzake; nalumikiza nsalu zisanu zina ina ndi inzake.


Ndipo onse a mtima waluso mwa iwo akuchita ntchitoyi anapanga chihema ndi nsalu zophimba khumi; anaziomba ndi bafuta wa thonje losansitsa, ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi akerubi, ntchito ya mmisiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa