Eksodo 36:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo analumikiza nsalu zisanu ina ndi inzake; nalumikiza nsalu zisanu zina ina ndi inzake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo analumikiza nsalu zisanu ina ndi inzake; nalumikiza nsalu zisanu zina ina ndi inzake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndipo adasokerera nsalu zisanu, kuti zikhale chinsalu chimodzi, zisanu zinazonso adazisokerera nkukhalanso chinsalu chimodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iwo analumikiza nsalu zisanu, kuti ikhale nsalu imodzi ndipo anachita chimodzimodzi ndi nsalu zisanu zinazo. Onani mutuwo |