Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo anaipangira mizati inai ya kasiya, nazikuta ndi golide; zokowera zao zinali zagolide; ndipo anaziyengera makamwa anai asiliva.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo anaipangira mizati inai ya kasiya, nazikuta ndi golide; zokowera zao zinali zagolide; ndipo anaziyengera makamwa anai asiliva.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Adapanga nsanamira zinai zakasiya zogwirizira nsalu yochingira ija. Nsanamirazo zinali zitakutidwa ndi golide, ndipo adaika ngoŵe zokoŵera ku nsanamirazo. Adapanga masinde anai asiliva ogwirizira nsanamirazo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Iwo anapanga nsanamira zinayi zamtengo wa mkesha zokutidwa ndi golide. Anapanganso ngowe zagolide za nsanamirazo ndi matsinde asiliva anayi.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:36
5 Mawu Ofanana  

ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Ndipo uziomba nsalu yotchinga ya thonje lamadzi, ndi lofiirira ndi lofiira, ndi la bafuta wa thonje losansitsa, aiombe ndi akerubi ntchito ya mmisiri;


Ndipo anaomba nsalu yotchinga ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa; anachiomba ndi akerubi ntchito ya mmisiri.


Ndipo anaomba nsalu yotsekera pa khomo la chihemacho, ya lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ntchito ya wopikula;


Chifukwa, taona, ndakuyesa iwe lero mzinda walinga, mzati wachitsulo, makoma amkuwa, padziko lonse, ndi pa mafumu a Yuda, ndi pa akulu ake, ndi pa ansembe ake, ndi pa anthu a m'dziko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa