Eksodo 36:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo anaomba nsalu yotchinga ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa; anachiomba ndi akerubi ntchito ya mmisiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo anaomba nsalu yotchinga ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa; anachiomba ndi akerubi ntchito ya mmisiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Pambuyo pake adapanga nsalu yochingira yobiriŵira, yofiirira ndi yofiira, ndiponso nsalu ya bafuta wosalala ndi wopikidwa bwino, ndipo adapetapo zithunzi za akerubi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Anapanga nsalu yokhala ndi mtundu wamtambo, wapepo ndi ofiira ndipo nsaluyo inali yolukidwa bwino, yofewa ndi yosalala. Ndipo anthu aluso anapetapo zithunzi za Akerubi. Onani mutuwo |