Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:37 - Buku Lopatulika

37 Ndipo anaomba nsalu yotsekera pa khomo la chihemacho, ya lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ntchito ya wopikula;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Ndipo anaomba nsalu yotsekera pa khomo la chihemacho, ya lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ntchito ya wopikula;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Pa chipata choloŵera m'chihemamo, adaikapo nsalu yochinga yobiriŵira, yofiirira ndi yofiira, ndiponso nsalu ya bafuta wosalala, wopikidwa bwino ndi wopetedwa mwaluso.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Anapanga nsalu ya pa chipata cholowera mu chihema, yamtundu wamtambo, wapepo ndi ofiira yomwe inali yofewa ndi yosalala, yopetedwa bwino ndi amisiri aluso.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:37
6 Mawu Ofanana  

ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ndi ubweya wa mbuzi;


Ndipo pa chipata cha bwalolo pakhale nsalu yotsekera ya mikono makumi awiri, ya lamadzi ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ntchito ya wopikula; nsichi zake zikhale zinai, ndi makamwa ao anai.


ndi guwa la nsembe lofukizapo, ndi mphiko zake, ndi mafuta odzoza, ndi chofukiza cha fungo lokoma, ndi nsalu yotsekera pakhomo, pa khomo la chihema;


Ndipo anaipangira mizati inai ya kasiya, nazikuta ndi golide; zokowera zao zinali zagolide; ndipo anaziyengera makamwa anai asiliva.


Ndipo anapachika pa chihema nsalu yotsekera pakhomo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa