Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo anapanga mitanda ya mtengo wakasiya; isanu ya matabwa a pa mbali ina ya chihema,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo anapanga mitanda ya mtengo wakasiya; isanu ya matabwa a pa mbali ina ya Kachisi,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Kenaka adapanga mitanda ya matabwa a mtengo wa kasiya, isanu ya mafulemu a mbali imodzi ya chihema,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Iwo anapanganso mitanda ya matabwa amtengo wa mkesha. Mitanda isanu inali ya maferemu a mbali imodzi ya chihema,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:31
6 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipanga mphiko za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi golide, kuti anyamulire nazo gome.


ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Ndipo upange mphiko za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi golide.


Ndipo panali matabwa asanu ndi atatu. Ndi makamwa ao asiliva, makamwa khumi kudza asanu ndi limodzi; makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi.


ndi mitanda isanu ya matabwa a pa mbali inzake ya chihema, ndi mitanda isanu ya matabwa a chihema ali pa mbali ya kumadzulo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa