Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo panali matabwa asanu ndi atatu. Ndi makamwa ao asiliva, makamwa khumi kudza asanu ndi limodzi; makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo panali matabwa asanu ndi atatu. Ndi makamwa ao asiliva, makamwa khumi kudza asanu ndi limodzi; makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Motero panali mafulemu asanu ndi atatu, ndi masinde asiliva 16, aŵiri pansi pa fulemu lililonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Choncho panali maferemu asanu ndi atatu ndiponso matsinde 16 asiliva, awiri anali pansi pa feremu iliyonse.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:30
3 Mawu Ofanana  

Ndipo pakhale matabwa asanu ndi atatu, ndi makamwa ao asiliva, ndiwo makamwa khumi mphambu asanu ndi limodzi; makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.


Ndipo anaphatikizika pamodzi patsinde, naphatikizika pamodzi pamutu pake ndi mphete imodzi; anatero nao onse awiri pangodya ziwiri.


Ndipo anapanga mitanda ya mtengo wakasiya; isanu ya matabwa a pa mbali ina ya chihema,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa