Eksodo 36:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo anaphatikizika pamodzi patsinde, naphatikizika pamodzi pamutu pake ndi mphete imodzi; anatero nao onse awiri pangodya ziwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo anaphatikizika pamodzi patsinde, naphatikizika pamodzi pamutu pake ndi mphete imodzi; anatero nao onse awiri pangodya ziwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Mafulemu aŵiri am'ngodyawo anali olumikizika pansi pake ndi ogwirizana mpaka pamwamba ku ngoŵe yokoŵera yoyamba ija. Ndimo m'mene mafulemu aŵiri opanga ngodya ziŵiri aja adapangidwira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Pa ngodya ziwirizi panali maferemu awiri, kuyambira pansi mpaka pamwamba atalumikizidwa pa ngowe imodzi. Maferemu onse anali ofanana. Onani mutuwo |