Eksodo 36:22 - Buku Lopatulika22 Pa thabwa limodzi panakhala mitsukwa iwiri, yomangika pamodzi; anawapanga momwemo matabwa onse a chihema. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Pa thabwa limodzi panakhala mitsukwa iwiri, yomangika pamodzi; anawapanga momwemo matabwa onse a Kachisi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Thabwa lililonse linali ndi zolumikizira ziŵiri, ndipo mafulemu onse adaŵapanga ndi zolumikizira ziŵiri. Mafulemu onse adaŵapanga ndi zolumikizira zotere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Thabwa lililonse linali ndi zolumikizira ziwiri. Iwo anapanga maferemu onse a chihemacho ndi matabwa otere. Onani mutuwo |