Eksodo 36:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo anapanga matabwa a chihema; matabwa makumi awiri a ku mbali ya kumwera, kumwera; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo anapanga matabwa a Kachisi; matabwa makumi awiri a ku mbali ya kumwera, kumwera; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Pa mbali yakumwera adapanga mafulemu makumi aŵiri, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Anapanga maferemu makumi awiri a mbali yakummwera kwa chihemacho, Onani mutuwo |