Eksodo 36:21 - Buku Lopatulika21 Utali wake wa thabwa limodzi ndiwo mikono khumi, ndi kupingasa kwake kwa thabwa limodzi ndiko mkono ndi hafu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Utali wake wa thabwa limodzi ndiwo mikono khumi, ndi kupingasa kwake kwa thabwa limodzi ndiko mkono ndi hafu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 M'litali mwa fulemu lililonse munali mamita anai ndi theka, ndipo muufupi mwake munali masentimita 69. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Feremu iliyonse inali yotalika mamita anayi ndipo mulifupi mwake munali masentimita 69. Onani mutuwo |