Eksodo 36:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo anapanga matabwa a chihema, oimirika, a mtengo wakasiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo anapanga matabwa a Kachisi, oimirika, a mtengo wakasiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Pambuyo pake adapanga mafulemu a chihemacho ndi matabwa a mtengo wa kasiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iwo anapanga maferemu amatabwa amtengo wa mkesha oyimikira chihemacho. Onani mutuwo |