Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo anasokera hemalo chophimba cha zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi chophimba cha zikopa za akatumbu pamwamba pake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo anasokera hemalo chophimba cha zikopa za nkhosa zamphongo zonika zofiira, ndi chophimba cha zikopa za akatumbu pamwamba pake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Ndipo adapanga chophimbira china chofiira cha zikopa za nkhosa zamphongo. Potsiriza adapanganso chophimbira china cha zikopa zofeŵa, nkuchiika pamwamba pa zophimba zina zonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Ndipo anapanga chikopa cha nkhosa zazimuna cha utoto wofiira chophimbira tentiyo ndipo pamwamba pake anapanganso chophimbira china cha zikopa za akatumbu.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:19
4 Mawu Ofanana  

ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Ndipo uzipangira hema chophimba cha zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi chophimba za zikopa za akatumbu pamwamba pake.


Ndipo anapanga zokowera makumi asanu zamkuwa kumanga pamodzi hemalo, kuti likhale limodzi.


Ndipo anapanga matabwa a chihema, oimirika, a mtengo wakasiya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa