Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo anamanga pamodzi nsalu zisanu pazokha, ndi nsalu zisanu ndi imodzi pazokha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo anamanga pamodzi nsalu zisanu pa zokha, ndi nsalu zisanu ndi imodzi pa zokha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Tsono adasokerera nsalu zisanu nkukhala chinsalu chimodzi, ndipo nsalu zinazo zisanu ndi imodzi, adazisokereranso kuti zikhale chinsalu chimodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Iwo analumikiza nsalu zisanu kukhala nsalu imodzi ndipo nsalu zinazo zisanu ndi imodzi, analumikizanso kukhala nsalu imodzinso.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:16
2 Mawu Ofanana  

Utali wake wa nsalu imodzi ndiwo mikono makumi atatu, ndi kupingasa kwake kwa nsalu imodzi ndiko mikono inai; nsalu khumi ndi imodzi zinafanana muyeso wao.


Ndipo anapanga magango makumi asanu m'mphepete mwa nsalu imodzi, ya kuthungo, ya chilumikizano, naika magango makumi asanu m'mphepete mwa nsalu ya kuthungo, ya chilumikizano china.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa