Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:15 - Buku Lopatulika

15 Utali wake wa nsalu imodzi ndiwo mikono makumi atatu, ndi kupingasa kwake kwa nsalu imodzi ndiko mikono inai; nsalu khumi ndi imodzi zinafanana muyeso wao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Utali wake wa nsalu imodzi ndiwo mikono makumi atatu, ndi kupingasa kwake kwa nsalu imodzi ndiko mikono inai; nsalu khumi ndi imodzi zinafanana muyeso wao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 M'litali mwa nsalu iliyonse munali mamita 14, ndipo muufupi mwake munali masentimita 183. Zonsezo zinali zofanana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Nsalu zonse khumi ndi imodzi zinali zofanana. Mulitali mwake munali mamita khumi ndi anayi ndipo mulifupi mwake munali mamita awiri.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:15
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anaomba nsalu zophimba za ubweya wa mbuzi zikhale chophimba pamwamba pa chihema; anaomba nsalu zophimba khumi ndi imodzi.


Ndipo anamanga pamodzi nsalu zisanu pazokha, ndi nsalu zisanu ndi imodzi pazokha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa