Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo anaomba nsalu zophimba za ubweya wa mbuzi zikhale chophimba pamwamba pa chihema; anaomba nsalu zophimba khumi ndi imodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo anaomba nsalu zophimba za ubweya wa mbuzi zikhale hema pamwamba pa Kachisi; anaomba nsalu zophimba khumi ndi imodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Pambuyo pake adasoka nsalu khumi ndi imodzi za ubweya wambuzi, napanga chophimbira pamwamba pa chihemacho.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Iwo anapanga nsalu za ubweya wambuzi zophimba pamwamba pa chihemacho. Nsalu zonse pamodzi zinalipo khumi ndi imodzi.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:14
2 Mawu Ofanana  

Utali wake wa nsalu imodzi ndiwo mikono makumi atatu, ndi kupingasa kwake kwa nsalu imodzi ndiko mikono inai; nsalu khumi ndi imodzi zinafanana muyeso wao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa