Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 36:12 - Buku Lopatulika

12 Anaika magango makumi asanu pansalu imodzi, naikanso magango makumi asanu m'mphepete mwake mwa nsalu ya chilumikizano china; magango anakomanizana lina ndi linzake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Anaika magango makumi asanu pa nsalu imodzi, naikanso magango makumi asanu m'mphepete mwake mwa nsalu ya chilumikizano china; magango anakomanizana lina ndi linzake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Adasoka magonga makumi asanu pa chinsalu choyambacho, ndi magonga ena makumi asanu pa chinsalu chinacho, mopenyana ndi magonga a chinsalu choyamba aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Iwo anasokerera zokolowekamo makumi asanu pa nsalu yoyamba ndi zokolowekamo makumi asanu zinanso pa nsalu inayo. Anapanga kuti zokolowekamozo ziziyangʼanana.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 36:12
4 Mawu Ofanana  

Ndipo uziika magango makumi asanu m'mphepete mwa nsalu imodzi, ya kuthungo ya chilumikizano, ndi magango makumi asanu m'mphepete mwa nsalu ya kuthungo ya chilumikizano china.


Ndipo uziika magango a nsalu ya madzi m'mphepete mwake mwa nsalu imodzi, ku mkawo wa chilumikizano; nuchite momwemo m'mphepete mwake mwa nsalu ya kuthungo ya chilumikizano china.


Uziika magango makumi asanu pansalu yochingira imodzi, nuikenso magango makumi asanu m'mphepete mwake mwa nsalu ya chilumikizano china; ndipo magango akomanizane lina ndi linzake.


Ndipo anaika magango ansalu yamadzi m'mphepete mwake mwa nsalu imodzi ku mkawo wa chilumikizano; nachita momwemo m'mphepete mwake mwa nsalu ya kuthungo, ya chilumikizano chachiwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa