Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 35:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Mose anasonkhanitsa khamu lonse la ana a Israele, nanena nao, Siwa mau amene Yehova analamula, kuti muwachite.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Mose anasonkhanitsa khamu lonse la ana a Israele, nanena nao, Siwa mau amene Yehova anauza, kuti muwachite.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mose adaitana Aisraele onse naŵauza kuti, “Chauta akukulamulani kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mose anasonkhanitsa gulu lonse la Aisraeli ndipo anawawuza kuti, “Zinthu zimene Yehova wakulamulirani kuti muzichite ndi izi:

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 35:1
7 Mawu Ofanana  

Udzikumbukira tsiku la Sabata, likhale lopatulika.


Ndipo atatero, ana onse a Israele anayandikiza; ndipo iye anawauza zonse Yehova adalankhula naye m'phiri la Sinai.


pakuti akumvaimva lamulo sakhala olungama pamaso pa Mulungu, koma akuchita lamulo adzayesedwa olungama.


Khalani akuchita mau, osati akumva okha, ndi kudzinyenga nokha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa