Eksodo 34:31 - Buku Lopatulika31 Koma Mose anawaitana; ndipo Aroni ndi akazembe onse a khamu la anthu anabwera kwa iye; ndipo Mose analankhula nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Koma Mose anawaitana; ndipo Aroni ndi akazembe onse a khamu la anthu anabwera kwa iye; ndipo Mose analankhula nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Koma Mose adaŵaitana, ndipo Aroni pamodzi ndi atsogoleri a Aisraele aja atabwera kwa iye, Moseyo adayamba kulankhula nawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Koma Mose anawayitana. Kotero Aaroni ndi atsogoleri onse a gululo anabwera kwa iye, ndipo anawayankhula. Onani mutuwo |