Eksodo 34:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo pamene Aroni ndi ana onse a Israele anaona Mose, taonani, khungu la nkhope yake linanyezimira; ndipo anaopa kumyandikiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo pamene Aroni ndi ana onse a Israele anaona Mose, taonani, khungu la nkhope yake linanyezimira; ndipo anaopa kumyandikiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Aroni ndi anthu onse aja atayang'ana Mose, adaona kuti nkhope yake njoŵala. Ndipo adachita mantha osafuna kumuyandikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Aaroni ndi Aisraeli ataona kuti nkhope ya Mose imanyezimira anaopa kumuyandikira. Onani mutuwo |