Eksodo 34:19 - Buku Lopatulika19 Onse oyambira kubadwa ndi anga; ndi zoweta zanu zonse zazimuna, zoyamba za ng'ombe ndi za nkhosa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Onse oyambira kubadwa ndi anga; ndi zoweta zanu zonse zazimuna, zoyamba za ng'ombe ndi za nkhosa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Mwana wamphongo aliyense woyamba kubadwa ndi wanga, pamodzi ndi wa zoŵeta yemwe, ndiye kuti ng'ombe ndi nkhosa zanu zomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 “Mwana aliyense woyamba kubadwa ndi wanga, pamodzi ndi ziweto zoyamba kubadwa zazimuna kuchokera ku ngʼombe kapena nkhosa. Onani mutuwo |