Eksodo 32:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo magomewo ndiwo ntchito ya Mulungu, kulembaku ndiko kulemba kwa Mulungu, kozokoteka pa magomewo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo magomewo ndiwo ntchito ya Mulungu, kulembaku ndiko kulemba kwa Mulungu, kozokoteka pa magomewo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Imeneyi inali ntchito ya Mulungu, ndipo zolembedwazo adaalemba ndi Mulungu mwini mozizokota pamiyalapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Miyalayi anayikonza ndi Mulungu. Malembawo analemba ndi Mulungu mozokota pa miyalapo. Onani mutuwo |