Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 31:8 - Buku Lopatulika

8 ndi gomelo ndi zipangizo zake, ndi choikaponyali choona ndi zipangizo zake, ndi guwa la nsembe lofukizapo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 ndi gomelo ndi zipangizo zake, ndi choikapo nyali choona ndi zipangizo zake, ndi guwa la nsembe lofukizapo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 tebulo ndi zipangizo zake, choikaponyale cha golide wabwino kwambiri, pamodzi ndi zipangizo zake, guwa lofukizirapo lubani,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 tebulo ndi zida zake, choyikapo nyale cha golide wabwino kwambiri ndi ziwiya zake zonse, guwa lofukizirapo lubani,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 31:8
5 Mawu Ofanana  

Akonze nyalizo pa choikaponyali choona pamaso pa Yehova nthawi zonse.


Kapena sayatsa nyali, ndi kuivundikira m'mbiya, koma aiika iyo pa choikapo chake; ndipo iunikira onse ali m'nyumbamo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa