Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 31:5 - Buku Lopatulika

5 ndi kuzokota miyala yoikika, ndi kozokota mtengo, kuchita ntchito zilizonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 ndi kuzokota miyala yoikika, ndi kozokota mtengo, kuchita ntchito zilizonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Akudziŵanso kuzokota miyala yogwira nayo ntchito, kujoba mitengo, ndi kuchita zaluso zonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 kusema ndi kuyika miyala yokongola, kukonza zinthu zamatabwa ndiponso kugwira ntchito ina iliyonse yamanja.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 31:5
4 Mawu Ofanana  

Koma ali nayo mphamvu ndani yakummangira Iye nyumba, popeza thambo lam'mwambamwamba silimfikira? Ndine yani ine tsono, kuti ndimmangire nyumba, koma kumfukizira chofukiza ndiko?


kulingirira ntchito zaluso, kuchita ndi golide ndi siliva ndi mkuwa,


Ndipo Ine, taona, ndampatsa Oholiyabu, mwana wa Ahisamaki, wa fuko la Dani, akhale naye; ndipo ndaika luso m'mitima ya onse a mtima waluso, kuti apange zonse ndakuuza iwe;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa