Eksodo 30:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo upange mphiko za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi golide. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo upange mphiko za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi golide. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mphiko zimenezi ikhale ya mtengo wa kasiya, ndipo uikute ndi golide. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Upange mizati yamtengo wa mkesha ndipo uyikute ndi golide. Onani mutuwo |