Eksodo 30:24 - Buku Lopatulika24 ndi kida mazana asanu, monga sekeli la malo opatulika, ndi mafuta a azitona hini limodzi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 ndi kida mazana asanu, monga sekeli la malo opatulika, ndi mafuta a azitona hini limodzi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 makilogaramu asanu ndi limodzi a kasiya (zonsezo potsata miyeso ya ku Nyumba ya Mulungu). Ndipo muwonjeze mafuta okwanira malita anai a olivi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 makilogalamu asanu ndi limodzi a mkesha. Zonsezi zikhale malingana ndi muyeso wa ku Nyumba ya Mulungu. Pakhalenso malita anayi a mafuta a olivi. Onani mutuwo |