Eksodo 30:14 - Buku Lopatulika14 Yense wakupita kwa owerengedwawo, wa zaka makumi awiri ndi wa mphambu zake, apereke choperekacho kwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Yense wakupita kwa owerengedwawo, wa zaka makumi awiri ndi wa mphambu zake, apereke choperekacho kwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Aliyense wolembedwa m'kalemberamo, wa zaka makumi aŵiri kapena kupitirira, adzapereke zimenezi kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Aliyense wolembedwa mu kawundula amene ali ndi zaka makumi awiri kapena kupitirira ayenera kupereka chopereka kwa Yehova. Onani mutuwo |