Eksodo 29:25 - Buku Lopatulika25 Pamenepo uzilandire m'manja mwao, ndi kuzipsereza paguwa la nsembe, pa nsembe yopsereza, zichite fungo lokoma pamaso pa Yehova; ndiyo nsembe yamoto ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Pamenepo uzilandire m'manja mwao, ndi kuzipsereza pa guwa la nsembe, pa nsembe yopsereza, zichite fungo lokoma pamaso pa Yehova; ndiyo nsembe yamoto ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Kenaka uchotse zonsezo m'manja mwao, ndipo uzipsereze pa guwa, pamwamba penipeni pa zopereka zija kuti zipereke fungo lokondweretsa Chauta. Imeneyi ndiyo nsembe yopsereza kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Kenaka uzitenge mʼmanja mwawo ndipo uzipsereze pa guwa lansembe, pamwamba penipeni pamodzi ndi nsembe yopsereza kuti ipereke fungo lokoma kwa Yehova. Ichi ndiye chopereka chachakudya kwa Yehova. Onani mutuwo |