Eksodo 29:24 - Buku Lopatulika24 ndipo uike zonsezi m'manja a Aroni, ndi m'manja a ana ake aamuna; nuziweyule nsembe yoweyula pamaso pa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 ndipo uike zonsezi m'manja a Aroni, ndi m'manja a ana ake amuna; nuziweyule nsembe yoweyula pamaso pa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Chakudya chonsechi uchiike m'manja mwa Aroni ndi mwa ana ake, ndipo iwowo achiweyule kuti chikhale chopereka choweyula kwa ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Izi zonse uzipereke mʼmanja mwa Aaroni ndi ana ake, ndipo iwo aziweyule pamaso pa Yehova kuti zikhale nsembe yoweyula. Onani mutuwo |